Eyiii yanga ija kunja kwacha Msanadzuke ndi tcheke FB Ndapeza meseji ya malama Ati wasowatu ase Ndati ize osadanda tigwilana pasanaduse mwezi Kenako dyaku wazahala Ati ndasowatu wezi ..ine shaa Apa mzanga wandithawapo koma ati tizakumana buddy
(Chorus) Ati life ndichoncho ase osamadanda Koma nanga ndiiwala bwanji friend Asalawa amakuonesa chikondi chabodza kuseli kumakujeda wezi Pomwe zibwana timapanga koma mijedo simbali yathu Poti mwati life ndichoncho Kwaife tingoti tizagwirana eee
(Verse 2) Pamene paja ndadandalapo zatha koma zkundivuta kuiwala wezi poti unali dyaku poselewulana paja zokwiyatu simbali yako eeeh Kenako ndati ndiyendeko ndazakumana nd faifiesi Basitu yathu ija zibwana tinthabwala mpaka takafika kutali wezi kuima pachiwaya komano cha mbalaga tiwaleko tsabola wezi umakwana umakwana iweyootu umakwana ase eee
(Chorus ) Ati life ndichoncho ase osamadanda Koma nanga ndiiwala bwanji friend Asalawa amakuonesa chikondi chabodza kuseli kumakujeda wezi Pomwe zibwana timapanga koma mijedo simbali yathu Poti mwati life ndichoncho Kwaife tingoti tizagwirana eee